2 Samueli 12:24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Davide anasangalatsa Bateseba mkazi wace, nalowa kwa iye, nagona naye; ndipo anabala mwana wamwamuna, namucha dzina lace Solomo. Ndipo Yehova anamkonda iye,

2 Samueli 12

2 Samueli 12:20-30