25. Ha! amphamvuwo anagwa pakati pa nkhondo!Jonatani anaphedwa pamisanje pako.
26. Ndipsinjika mtima cifukwa ca iwe, mbale wanga Jonatani;Wandikomera kwambiri;Cikondi cako, ndinadabwa naco,Cinaposa cikondi ca anthu akazi.
27. Ha! amphamvuwo anagwa,Ndi zida za nkhondo zinaonengeka,