2 Mbiri 8:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo kunali, zitatha zaka makumi awiri m'mene anamanga nyumba ya Yehova, ndi nyumba yace yace,

2. Solomo anamanga midzi imene Huramu adampatsa, nakhalitsamo ana a Israyeli.

3. Ndipo Solomo anamuka ku Hamati Zoba, naugonjetsa.

4. Ndipo anamanga Tadimori m'cipululu, ndi midzi yonse yosungiramo cuma, imene anaimanga m'Hamati.

2 Mbiri 8