2 Mbiri 3:10-12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

10. Ndipo m'malo opatulikitsa anapanga akerubi awiri, anacita osema, nawakuta ndi golidi.

11. Ndi mapiko a akerubi m'litali mwace ndimo mikono makumi awiri; phiko la kerubi mmodzi mikono isanu, lojima khoma la nyumba; ndi phiko linzace mikono isanu, lokhudzana nalo phiko la kerubi wina.

12. Ndi phiko la kerubi wina mikono isanu lojima khoma la nyumba, ndi phiko linzace mikono isanu lolumikizana ndi phiko la kerubi wina.

2 Mbiri 3