2 Mafumu 9:26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndapenyadi dzulo mwazi wa Naboti ndi mwazi wa ana ace, ati Yehova; ndipo ndikubwezera pamunda pano, ati Yehova, Mtengeni tsono, mumponye pamundapo, monga mwa mau a Yehova.

2 Mafumu 9

2 Mafumu 9:22-29