2 Mafumu 7:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anawalondola mpaka ku Yordano; ndipo taonani, m'njira monse munadzala ndi zobvala ndi akatundu adazitaya Aaramu m'kufulumira kwao. Nibwera mithenga, nifotokozera mfumu.

2 Mafumu 7

2 Mafumu 7:9-20