2 Mafumu 3:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Napasula midzi, naponya yense mwala wace panthaka ponse pabwino, naidzaza, nafotsera zitsime zonse zamadzi, nagwetsa mitengo yonse yabwino, kufikira anasiya miyala yace m'Kirihasereti mokha; koma oponya miyala anauzinga, naukantha.

2 Mafumu 3

2 Mafumu 3:21-27