2 Mafumu 23:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Anatinso, Cizindikilo ici ndiciona nciani? Namuuza anthu a m'mudziwo, Ndico manda a munthu wa Mulungu anafuma ku Yuda, nalalikira izi mwazicitira guwa la nsembe la ku Beteli.

2 Mafumu 23

2 Mafumu 23:11-18