2 Mafumu 23:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo potembenuka Yosiya anaona manda okhalako kuphiri, natumiza anthu naturutsa mafupa kumanda, nawatentha pa guwa la nsembe, kuliipitsa, monga mwa mau a Yehova anawalalikira munthu wa Mulungu wolalikira izi.

2 Mafumu 23

2 Mafumu 23:7-22