2 Mafumu 18:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Anacotsa misanje, naphwanya zoimiritsa, nalikha cifanizo, naphwanya njoka ija yamkuwa adaipanga Mose; pakuti kufikira masiku awa ana a Israyeli anaifukizira zonunkhira, naicha Cimkuwa.

2 Mafumu 18

2 Mafumu 18:1-10