2 Mafumu 11:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma Yehoyada wansembe analamulira atsogoleri a mazana oyang'anira khamu, nanena nao, Mumturutse mkaziyo pabwalo pakati pa mipambo; womtsata iye mumuphe ndi lupanga; pakuti wansembe adati, Asaphedwe m'nyumba ya Yehova.

2 Mafumu 11

2 Mafumu 11:7-18