2 Akorinto 12:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kuti ndingakwezeke koposa, cifukwa ca ukulu woposa wa mabvumbulutso, kunapatsidwa kwa ine munga m'thupi, ndiye mngelowa Satana kutianditundudze, kuti ndingakwezeke koposa.

2 Akorinto 12

2 Akorinto 12:3-16