1 Yohane 4:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Umo muli cikondi, sikuti ife tinakonda Mulungu, koma kuti iye anatikonda ife, ndipo anatuma Mwana wace akhale ciombolo cifukwa ca macime athu.

1 Yohane 4

1 Yohane 4:5-12