1 Samueli 30:26-28 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

26. Ndipo pamene Davide anafika ku Zikilaga, anatumizako za zofunkhazo kwa akuru a Yuda, ndiwo abwenzi ace, nati, Siyi mphatso yanu ya zofunkha za adani a Yehova.

27. Anatumiza kwa iwo a ku Beteli, ndi kwa iwo a ku Ramoti wa kumwela, ndi kwa iwo a ku Yatiri;

28. ndi kwa iwo a ku Aroeri, ndi kwa iwo a ku Sifimoti, ndi kwa iwo a ku Estimoa;

1 Samueli 30