1 Samueli 30:26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pamene Davide anafika ku Zikilaga, anatumizako za zofunkhazo kwa akuru a Yuda, ndiwo abwenzi ace, nati, Siyi mphatso yanu ya zofunkha za adani a Yehova.

1 Samueli 30

1 Samueli 30:19-29