1 Samueli 30:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Davide anawakantha kuyambira madzulo kufikira usiku wa mawa wace; ndipo panalibe munthu mmodzi wa iwowa anapulumuka, koma anyamata mazana anai oberekeka pa ngamila, nathawa.

1 Samueli 30

1 Samueli 30:8-26