1 Samueli 28:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pomwepo Sauli anagwa pansi tantha, naopa kwakukuru, cifukwa ca mau a Samueli; ndipo analibe mphamvu; pakuti tsiku lonse ndi usiku wace wonse anakhala osadya kanthu.

1 Samueli 28

1 Samueli 28:16-23