1 Samueli 23:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo iye ananena naye, Usaopa; cifukwa dzanja la Sauli atate wanga silidzakupeza; iwe udzakhala mfumu ya Israyeli, ndipo ine ndidzakhala wotsatana nawe, icinso Sauli atate wanga acidziwa.

1 Samueli 23

1 Samueli 23:13-21