1 Samueli 18:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anyamata a Sauli analankhula mau awa m'makutu a Davide. Nati Davide, Kodi muciyesera cinthu copepuka kukhala mkamwini wa mfumu, popeza ndiri munthu wosauka, ndi wopeputsidwa.

1 Samueli 18

1 Samueli 18:22-27