40. Ndipo mwana wa Yonatani ndiye Meribaala; ndi Meribaala anabala Mika.
41. Ndi ana a Mika: Pitoni, ndi Meleki, ndi Tareya, ndi Ahazi.
42. Ndi Ahazi anabala Yara, ndi Yara anabala Ameleti, ndi Azmaveti, ndi Zimri; ndi Zimri anabala Moza,
43. ndi Moza anabala Bineya, ndi Refaya mwana wace, Eleasa mwana wace; Azeli mwana wace;