1 Mbiri 8:40 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ana a Ulamu ndiwo ngwazi zamphamvu, ndiwo oponya mibvi, nakhala nao ana ambiri ndi zidzukulu zana limodzi. Onsewa ndiwo a ana a Benjamini.

1 Mbiri 8

1 Mbiri 8:31-40