1 Mbiri 8:38 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo Azeli anali nao ana asanu ndi mmodzi, maina ao ndiwo Azrikamu, Bokeru, ndi Ismayeli, ndi Seariya, ndi Obadiya, ndi Hanani. Onsewa ndiwo ana a Azeli.

1 Mbiri 8

1 Mbiri 8:32-40