1 Mbiri 4:42 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ena a iwowa a ana a Simeoni, amuna mazana asanu, anamka ku phiri la Seiri; akuwatsogolera ndiwo Pelatiya, ndi Neariya, ndi Refaya, ndi Uzieli; ana a lsi.

1 Mbiri 4

1 Mbiri 4:40-43