1 Mbiri 23:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anawerengedwa Alevi oyambira zaka makumi atatu ndi mphambu, ndipo ciwerengo cao kuwawerenga mmodzi mmodzi ndico amuna zikwi makumi atatu mphambu zisanu ndi zitatu.

1 Mbiri 23

1 Mbiri 23:1-8