1 Mbiri 18:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Davide anaika asilikari a boma m'Aramu wa Damasiko; ndi Aaramu anasanduka anthu a Davide, nabwera nazo mphatso, Ndipo Yehova anasunga Davide kuli konse anamukako.

1 Mbiri 18

1 Mbiri 18:2-7