1 Mbiri 17:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti Inu, Mulungu wanga, mwaululira mtumiki wanu kuti mudzammangira banja; momwemo mtumiki wanu waona mtima wakupemphera pamaso panu.

1 Mbiri 17

1 Mbiri 17:21-27