1 Mbiri 12:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Anadzawo kwa Davide ku Zikilaga, akali citsekedwere cifukwa ca Sauli mwana wa Kisi, ndi awa; ndiwo mwa amphamvuwo omthandiza kunkhondo.

1 Mbiri 12

1 Mbiri 12:1-6