1 Mbiri 11:41-47 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

41. Uriya Mhiti, Zabadi mwana wa Alai,

42. Adina mwana wa Siza Mrubeni mkuru wa Arubeni, ndi makumi atatu pamodzi naye,

43. Hanani mwana wa Maaka, ndi Yosafati Mmitini,

44. Uziya M-asterati, Sama ndi Yeieli ana a Hotamu wa ku Aroeri,

45. Yedyaeli mwana wa Simri, ndi Yoha mbale wace Mtizi,

46. Elieli Mmahavi, ndi Yeribai ndi Yosaviya ana a Elinaamu, ndi Itima Mmoabu,

47. Elieli, ndi Obedi, ndi Yasiyeli Mmezobai.

1 Mbiri 11