1 Mbiri 1:31-35 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

31. Hadada, ndi Tema, Nafisi, ndi Kedema. Awa ndi ana a Ismayeli.

32. Ndi ana a Ketura mkazi wamng'ono wa Abrahamu anabala Zimiramu, ndi Yokisani, ndi Medani, ndi Midyani, ndi Isibaki, ndi Sua. Ndi ana a Yokisani: Seba, ndi Dedani.

33. Ndi ana a Midyani: Efa, ndi Eferi, ndi Hanoki, ndi Abida, ndi Elidaa. Awa onse ndiwo ana a Ketura.

34. Ndipo Abrahamu anabala Isake. Ana a Isake: Esau, ndi Israyeli.

35. Ana a Esau: Elifazi, Reueli, ndi Yeuzi, ndi Yolamu, ndi Kora.

1 Mbiri 1