1 Mbiri 1:27-37 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

27. Abramu, (ndiye Abrahamu).

28. Ana a Abrahamu: Isake, ndi Ismayeli.

29. Mibadwo yao ndi awa; woyamba wa Ismayeli Nebayoti; ndi Kedara ndi Adibeli, ndi Mibisamu,

30. Misma, ndi Duma Masa,

31. Hadada, ndi Tema, Nafisi, ndi Kedema. Awa ndi ana a Ismayeli.

32. Ndi ana a Ketura mkazi wamng'ono wa Abrahamu anabala Zimiramu, ndi Yokisani, ndi Medani, ndi Midyani, ndi Isibaki, ndi Sua. Ndi ana a Yokisani: Seba, ndi Dedani.

33. Ndi ana a Midyani: Efa, ndi Eferi, ndi Hanoki, ndi Abida, ndi Elidaa. Awa onse ndiwo ana a Ketura.

34. Ndipo Abrahamu anabala Isake. Ana a Isake: Esau, ndi Israyeli.

35. Ana a Esau: Elifazi, Reueli, ndi Yeuzi, ndi Yolamu, ndi Kora.

36. Ana a Elifazi: Teani, ndi Omara, Zefi, ndi Gatamu, Kenazi, ndi Timna, ndi Amaleki.

37. Ana a Reueli: Nahati, Zera, Sama, ndi Miza.

1 Mbiri 1