25. Eberi, Pelegi, Reu,
26. Serugi, Nahori, Tera;
27. Abramu, (ndiye Abrahamu).
28. Ana a Abrahamu: Isake, ndi Ismayeli.
29. Mibadwo yao ndi awa; woyamba wa Ismayeli Nebayoti; ndi Kedara ndi Adibeli, ndi Mibisamu,
30. Misma, ndi Duma Masa,
31. Hadada, ndi Tema, Nafisi, ndi Kedema. Awa ndi ana a Ismayeli.
32. Ndi ana a Ketura mkazi wamng'ono wa Abrahamu anabala Zimiramu, ndi Yokisani, ndi Medani, ndi Midyani, ndi Isibaki, ndi Sua. Ndi ana a Yokisani: Seba, ndi Dedani.