1 Mafumu 7:40 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Hiramu anayenga mbiyazo ndi zoolera ndi mbale zowazira. Motero Hiramu anatsiriza kupanga nchito yonse anaicitira mfumu Solomo ya m'nyumba ya Yehova.

1 Mafumu 7

1 Mafumu 7:35-49