46. Ndipo anacotsa m'dziko anyamata onyansa aja adatsalira masiku a atate wace Asa.
47. Ndipo m'Edomu munalibe mfumu, koma kazembe wa mfumu.
48. Yehosafati anamanga zombo za ku Tarsisi kukatenga golidi ku Ofiri; koma sizinamuka, popeza zinaphwanyika pa Ezioni Geberi.