1 Mafumu 21:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yezebeli mkazi wace anati kwa iye, Kodi mulamulira Aisrayeli tsopano ndinu? Taukani, idyani mkate, ukondwere mtima wanu; munda wa Naboti wa ku Yezreeli ndidzakupatsani ndine.

1 Mafumu 21

1 Mafumu 21:1-14