1 Mafumu 21:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nati kwa iye, Popeza ndinalankhula kwa Naboti wa ku Yezreeli, ndinati kwa iye, Undigulitse munda wako ndi ndalama; kapena ukafuna, ndikupatsa munda wina m'malo mwace; kama anandiyankha, Sindikupatsani munda wanga wamphesa.

1 Mafumu 21

1 Mafumu 21:1-12