1 Mafumu 16:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma anthu akutsata Omri anapambana iwo akutsata Tibini mwana wa Ginati; nafa Tibini, Omri nakhala mfumu.

1 Mafumu 16

1 Mafumu 16:20-28