1 Mafumu 13:32 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Popeza mau aja anawapfuula mwa mau a Yehova kutemberera guwa la nsembe la ku Beteli, ndi kutemberera nyumba zonse za misanje iri m'midzi ya ku Samariya, adzacitika ndithu.

1 Mafumu 13

1 Mafumu 13:27-34