1 Mafumu 1:35 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo mumtsate iye, iye nadzadza nadzakhala pa mpando wanga wacifumu, popeza adzakhala iyeyu mfumu m'malo mwanga; ndipo ndamuika iye akhale mtsogoleri wa lsrayeli ndi Yuda.

1 Mafumu 1

1 Mafumu 1:34-37