1 Atesalonika 2:19-20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

19. Pakuti ciyembekezo cathu, kapena cimwemwe, kapena korona wakudzitamandira naye nciani? si ndinu nanga pamaso pa Ambuye wathu Yesu m'kufika kwace?

20. Pakuti inu ndinu ulemerero wathu ndi cimwemwe cathu.

1 Atesalonika 2