1 Akorinto 14:24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma ngati onse anenera, ndipo alowamo wina wosakhulupirira kapena wosaphunzira, atsutsidwa ndi onse; aweruzidwa ndi onse;

1 Akorinto 14

1 Akorinto 14:15-28