Zekariya 14:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kudzali tsiku lomwelo, kuti cisokonezo cacikuru cocokera kwa Yehova cidzakhala pakati pao; ndipo adzagwira yense dzanja la mnzace; ndi dzanja lace lidzaukira dzanja la mnzace.

Zekariya 14

Zekariya 14:3-20