Zekariya 11:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

M'mwemo ndinadyetsa zoweta zakukaphedwa, ndizo zoweta zonyankhalala. Ndipo ndinadzitengera ndodo ziwiri; yina ndinaicha Cisomo, inzace ndinaicha Comanganitsa; ndipo ndinadyetsa zowetazo.

Zekariya 11

Zekariya 11:1-17