Zefaniya 3:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Yehova pakati pace ali wolungama; sadzacita cosalungama, m'mawa ndi m'mawa aonetsera ciweruzo cace poyera, cosasowa kanthu; koma wosalungama sadziwa manyazi.

Zefaniya 3

Zefaniya 3:1-12