Zefaniya 2:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Tsoka, okhala m'dziko la kunyanja, mtundu wa Akereti! Mau a Yehova atsutsana nawe, Kanani, dziko la Afilisti; ndidzakuononga, kuti pasakhale wokhala m'dziko.

Zefaniya 2

Zefaniya 2:1-12