Zefaniya 1:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Tsikulo ndi tsiku la mkwiyo, tsiku la msauko ndi lopsinja tsiku la bwinja, ndi cipasuko, tsiku la mdima ndi la cisisira, tsiku la mitambo ndi lakuda bii;

Zefaniya 1

Zefaniya 1:8-18