Yoweli 3:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Aigupto adzasanduka bwinja, ndi Edomu adzasanduka cipululu copanda kanthu, cifukwa ca ciwawaci anawacitira ana a Yuda; popeza anakhetsa mwazi wosacimwa m'dziko lao.

Yoweli 3

Yoweli 3:13-21