Yoweli 3:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova adzadzuma ali ku Ziyoni, ndi kumveketsa mau ace ali ku Yerusalemu; ndi thambo ndi dziko lapansi zidzagwedezeka; koma Yehova adzakhala copulumukirako anthu ace, ndi linga la ana a Israyeli.

Yoweli 3

Yoweli 3:10-21