Yoweli 2:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Moto unyambita pamaso pao, ndi m'mbuyo mwao litentha lawi la moto; kumaso kwao dziko likunga munda wa Edeni, koma m'mbuyo mwao likunga cipululu copanda kanthu; palibenso wakuwapulumuka.

Yoweli 2

Yoweli 2:1-9