Yoweli 1:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Patulani tsiku losala, lalikirani masonkhano oletsa, sonkhanitsani akulu akulu, ndi onse okhala m'dziko, ku nyumba ya Yehova Mulungu wanu; nimupfuulire kwa Yehova.

Yoweli 1

Yoweli 1:8-20