Yoswa 8:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamene amuna a ku Ai anaceuka, anapenya, ndipo taonani, utsi wa mudzi unakwera kumwamba; nasowa mphamvu iwo kuthawa cakuno kapena cauko; ndi anthu othawira kucipululu anatembenukira owapitikitsa.

Yoswa 8

Yoswa 8:18-28